1 Samueli 2:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Koma Samueli ankakula bwino ndipo ankakondedwa kwambiri ndi Yehova komanso anthu.+ 1 Samueli 3:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Samueli anapitiriza kukula ndipo Yehova anali naye,+ moti palibe mawu ake alionse amene sanakwaniritsidwe.
19 Samueli anapitiriza kukula ndipo Yehova anali naye,+ moti palibe mawu ake alionse amene sanakwaniritsidwe.