Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Kenako Davide anathamanga nʼkukaima pambali pake. Atatero anasolola lupanga la Mfilisitiyo+ mʼchimake nʼkumudula mutu pofuna kutsimikizira kuti wafadi. Afilisiti ataona kuti ngwazi yawo yamphamvu ija yafa, anayamba kuthawa.+

  • 1 Samueli 17:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Kenako Davide anatenga mutu wa Mfilisiti uja nʼkupita nawo ku Yerusalemu koma zida za Mfilisitiyo anaziika mutenti yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena