1 Mafumu 2:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Choncho Solomo anachotsa Abiyatara kuti asatumikirenso monga wansembe wa Yehova ndipo izi zinakwaniritsa mawu amene Yehova analankhula ku Silo+ okhudza nyumba ya Eli.+ 1 Mafumu 2:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Zitatero, mfumu inasankha Benaya+ mwana wa Yehoyada kuti akhale mkulu wa asilikali mʼmalo mwa Yowabu, ndipo inasankha wansembe Zadoki+ kuti alowe mʼmalo mwa Abiyatara. 1 Mbiri 29:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Pa tsikulo, iwo anadya ndi kumwa mosangalala kwambiri+ pamaso pa Yehova. Kachiwirinso, anaveka Solomo mwana wa Davide ufumu ndipo anamudzoza pamaso pa Yehova kukhala mtsogoleri.+ Anadzozanso Zadoki kukhala wansembe.+
27 Choncho Solomo anachotsa Abiyatara kuti asatumikirenso monga wansembe wa Yehova ndipo izi zinakwaniritsa mawu amene Yehova analankhula ku Silo+ okhudza nyumba ya Eli.+
35 Zitatero, mfumu inasankha Benaya+ mwana wa Yehoyada kuti akhale mkulu wa asilikali mʼmalo mwa Yowabu, ndipo inasankha wansembe Zadoki+ kuti alowe mʼmalo mwa Abiyatara.
22 Pa tsikulo, iwo anadya ndi kumwa mosangalala kwambiri+ pamaso pa Yehova. Kachiwirinso, anaveka Solomo mwana wa Davide ufumu ndipo anamudzoza pamaso pa Yehova kukhala mtsogoleri.+ Anadzozanso Zadoki kukhala wansembe.+