Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 23:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Awa ndi mayina a asilikali amphamvu a Davide:+ Yosebu-basebete mbadwa ya Hakemoni, mtsogoleri wa amuna atatu.+ Iye anatenga mkondo wake nʼkupha anthu 800 nthawi imodzi.

  • 2 Samueli 23:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 ndi Uriya+ Muhiti, onse pamodzi analipo 37.

  • 1 Mafumu 15:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anatero popeza Davide anachita zoyenera pamaso pa Yehova, ndipo anatsatira chilichonse chimene Mulungu anamulamula masiku onse a moyo wake, kupatulapo pa nkhani ya Uriya Muhiti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena