Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 12:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova wanena kuti, ‘Ndikugwetsera tsoka kuchokera mʼnyumba yako+ yomwe komanso iwe ukuona. Ndidzatenga akazi ako nʼkuwapereka kwa mwamuna wina,+ ndipo iye adzagona ndi akazi akowo masanasana.+

  • 2 Samueli 16:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ahitofeli anauza Abisalomu kuti: “Ugone ndi akazi aangʼono* a bambo ako+ amene awasiya kuti azisamalira nyumba.*+ Ukatero Aisiraeli onse adzamva kuti wadzinunkhitsa pamaso pa bambo ako, ndipo udzapatsa mphamvu anthu amene ali kumbali yako.”

  • 2 Samueli 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mfumu Davide atafika kunyumba yake* ku Yerusalemu,+ anatenga akazi ake aangʼono 10, amene anawasiya kuti azisamalira nyumba yake aja+ nʼkuwatsekera mʼnyumba ina ndipo anaikapo alonda. Iye ankawapatsa chakudya koma sanagone nawo.+ Iwo anapitiriza kukhala mʼnyumbamo mpaka tsiku limene anamwalira. Ankakhala ngati akazi amasiye ngakhale kuti mwamuna wawo anali moyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena