Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Iwo alinso ndi ana awo awiri komweko, Ahimazi+ mwana wa Zadoki ndi Yonatani+ mwana wa Abiyatara. Ndiye mukatume ana awowo kuti adzandiuze zonse zimene mungamve.”

  • 2 Samueli 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiye tumizani uthenga mwamsanga kwa Davide wakuti, ‘Usiku uno musakhale pamalo owolokera kuchipululu. Koma muwoloke ndithu chifukwa mukapanda kutero inu mfumu ndi anthu onse amene muli nawo, muphedwa.’”+

  • 2 Samueli 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anthuwo atachoka, Ahimazi ndi Yonatani anatuluka mʼchitsimemo nʼkupita kukauza Mfumu Davide kuti: “Nyamukani mwamsanga ndipo muwoloke mtsinje.” Kenako anawauza malangizo amene Ahitofeli anapereka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena