-
Genesis 43:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Ndiyeno bambo awo Isiraeli anawauza kuti: “Ngati ndi choncho, chitani izi: Tengani zinthu zamtengo wapatali zamʼdziko lino mʼmatumba anu, mukamʼpatse munthuyo monga mphatso.+ Tengani mafuta a basamu+ pangʼono, uchi pangʼono, labidanamu, khungwa la utomoni wonunkhira,+ mtedza wa pisitasho ndi zipatso za amondi.
-