Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yezebeli atamva zimenezo, anatuma munthu kwa Eliya kukamuuza kuti: “Milungu yanga indilange mowirikiza, ngati pofika nthawi ino mawa sindidzakhala nditakupha ngati mmene waphera aneneriwo.”

  • Aroma 11:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mulungu sanakane anthu ake amene anali oyambirira kuwavomereza.+ Kodi simukudziwa zimene lemba lina limanena zokhudza Eliya, pamene anachonderera Mulungu motsutsa Aisiraeli? Limati: 3 “Yehova,* iwo apha aneneri anu ndipo agwetsa maguwa anu ansembe moti ine ndatsala ndekhandekha. Tsopano ayambanso kundifunafuna kuti andiphe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena