Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 8:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Elisa anapita ku Damasiko+ ndipo pa nthawiyo nʼkuti Beni-hadadi+ mfumu ya Siriya akudwala. Choncho mfumuyo inauzidwa kuti: “Munthu wa Mulungu woona+ uja wabwera kuno.” 8 Mfumuyo itamva zimenezi, inauza Hazaeli+ kuti: “Tenga mphatso ndipo upite kwa munthu wa Mulungu woonayo.+ Ukafunse kwa Yehova kudzera mwa iye kuti, ‘Kodi ndichira matenda angawa?’”

  • Amosi 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndidzatumiza moto panyumba ya Hazaeli,+

      Ndipo udzawotcheratu nsanja zolimba za Beni-hadadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena