Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno ana a aneneri* amene anali ku Beteli anabwera kwa Elisa nʼkumufunsa kuti: “Kodi ukudziwa kuti lero Yehova atenga mbuye wako kuti asakhalenso mtsogoleri wako?”+ Iye anayankha kuti: “Ndikudziwa zimenezo. Khalani chete.”

  • 2 Mafumu 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako ana a aneneri amene anali ku Yeriko anapita kwa Elisa nʼkumufunsa kuti: “Kodi ukudziwa kuti lero Yehova atenga mbuye wako kuti asakhalenso mtsogoleri wako?” Iye anayankha kuti: “Ndikudziwa zimenezo. Khalani chete.”

  • 2 Mafumu 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mneneri Elisa anaitana mmodzi wa ana a aneneri nʼkumuuza kuti: “Manga zovala zako mʼchiuno, nyamula botolo ladothi la mafutali ndipo upite mwamsanga ku Ramoti-giliyadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena