Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Beni-hadadi+ mfumu ya Siriya+ anasonkhanitsa asilikali ake onse. Atatero ananyamuka pamodzi ndi mafumu ena 32 ndi mahatchi komanso magaleta awo ndipo anapita kukazungulira mzinda+ wa Samariya+ nʼkuyamba kumenyana nawo.

  • 1 Mafumu 20:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Beni-hadadi anauza Ahabu kuti: “Ndibweza mizinda imene bambo anga analanda bambo anu ndipo mukhoza kukhazikitsa misika* ku Damasiko ngati mmene bambo anga anachitira ku Samariya.”

      Ahabu anayankha kuti: “Tikapanga pangano loti zikhaladi chonchi, ndikusiya kuti uzipita kwanu.”

      Atatero anachita naye pangano ndipo anamusiya kuti azipita.

  • 1 Mafumu 22:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Mfumu ya Siriya inali italamula akuluakulu 32 oyangʼanira asilikali okwera magaleta kuti:+ “Musakamenyane ndi wina aliyense, wamngʼono kapena wamkulu, koma mfumu ya Isiraeli yokha basi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena