2 Mafumu 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pamene ankayenda, uku akulankhulana, anangoona galeta* lankhondo lowala ngati moto ndi mahatchi* owala ngati moto.+ Galeta ndi mahatchiwo zinadutsa pakati pawo nʼkuwalekanitsa ndipo Eliya anatengedwa mumphepo yamkuntho nʼkupita kumwamba.*+ Salimo 68:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Magaleta ankhondo a Mulungu ali mʼmagulu a masauzande osawerengeka, ali mʼmagulu masauzandemasauzande.+ Yehova walowa mʼmalo oyera kuchokera kuphiri la Sinai.+ Zekariya 6:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Kenako nditayangʼananso kumwamba ndinaona magaleta 4 akubwera kuchokera pakati pa mapiri awiri. Mapiriwo anali akopa.*
11 Pamene ankayenda, uku akulankhulana, anangoona galeta* lankhondo lowala ngati moto ndi mahatchi* owala ngati moto.+ Galeta ndi mahatchiwo zinadutsa pakati pawo nʼkuwalekanitsa ndipo Eliya anatengedwa mumphepo yamkuntho nʼkupita kumwamba.*+
17 Magaleta ankhondo a Mulungu ali mʼmagulu a masauzande osawerengeka, ali mʼmagulu masauzandemasauzande.+ Yehova walowa mʼmalo oyera kuchokera kuphiri la Sinai.+
6 Kenako nditayangʼananso kumwamba ndinaona magaleta 4 akubwera kuchokera pakati pa mapiri awiri. Mapiriwo anali akopa.*