Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 11:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndiyeno Yehoyada anachita pangano pakati pa Yehova, mfumu ndi anthu,+ kuti iwo apitiriza kukhala anthu a Yehova. Anachitanso pangano pakati pa mfumu ndi anthuwo.+ 18 Kenako anthu onse amʼdzikolo anapita kukachisi wa Baala nʼkukagwetsa maguwa ake ansembe,+ kuphwanyaphwanya mafano ake+ komanso anapha wansembe wa Baala+ dzina lake Mateni kutsogolo kwa maguwa ansembewo.

      Ndiyeno wansembe Yehoyada anasankha anthu kuti aziyangʼanira nyumba ya Yehova.+

  • 2 Mbiri 34:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yosiya+ anayamba kulamulira ali ndi zaka 8 ndipo analamulira zaka 31 ku Yerusalemu.+

  • 2 Mbiri 34:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Mfumuyo inaimirira pamalo ake ndipo inachita* pangano+ pamaso pa Yehova, kuti idzatsatira Yehova ndi kusunga malamulo ake ndiponso zikumbutso zake. Inanena kuti idzachita zimenezi ndi mtima wake wonse+ ndi moyo wake wonse potsatira mawu a pangano olembedwa mʼbukulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena