Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno Davide anawagawa mʼmagulu+ mogwirizana ndi ana a Levi: Gerisoni, Kohati ndi Merari.+

  • 1 Mbiri 23:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Mʼmawa uliwonse ankaimirira+ kuti athokoze ndi kutamanda Yehova. Madzulo ankachitanso zimenezi.+ 31 Ankathandizanso pa nthawi iliyonse yopereka nsembe zopsereza kwa Yehova pa Masabata,+ pa masiku amene mwezi watsopano waoneka+ ndi pa nthawi ya zikondwerero.+ Ankachita zimenezi nthawi zonse pamaso pa Yehova, malinga ndi ziwerengero zake zogwirizana ndi malamulo ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena