Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 12:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo ankapereka ndalama zimene awerengazo kwa anthu amene ankayangʼanira ntchito yokonza nyumba ya Yehova. Anthuwo ankagwiritsa ntchito ndalamazo polipira akalipentala, anthu omwe ankagwira ntchito yomanga panyumba ya Yehovayo,+ 12 amisiri omanga ndi miyala ndi anthu osema miyala. Ndalamazo anaguliranso matabwa ndi miyala yosema yokonzera nyumba ya Yehova ndiponso analipirira zonse zimene anagwiritsa ntchito pokonza nyumbayo.

  • 2 Mbiri 34:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako ndalamazo anazipereka kwa anthu amene anasankhidwa kuti aziyangʼanira ntchito panyumba ya Yehova. Ndiyeno anthu amene ankagwira ntchito panyumba ya Yehova anagwiritsa ntchito ndalamazo pokonza nyumbayo. 11 Anthu ogwira ntchitowa anapereka ndalamazo kwa amisiri ndi kwa omanga nyumba kuti agulire miyala yosema komanso matabwa olimbitsira nyumba ndiponso kuti akhome mitanda ya nyumba zimene mafumu a Yuda anazilekerera kuti ziwonongeke.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena