Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 28:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anamupatsanso mapulani a kamangidwe ka zonse zimene anauzidwa kudzera mwa mzimu zokhudza mabwalo+ a nyumba ya Yehova, zipinda zonse zodyera kuzungulira kachisi, mosungira chuma cha nyumba ya Mulungu woona ndi mosungira zinthu zimene anaziyeretsa kuti zikhale zopatulika.+ 13 Komanso anamʼpatsa malangizo okhudza magulu a ansembe+ ndi a Alevi, ntchito yonse yokhudza utumiki wapanyumba ya Yehova ndiponso malangizo okhudza ziwiya zonse za utumiki wapanyumba ya Yehova.

  • 2 Mbiri 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kenako Solomo anapereka nsembe zopsereza+ kwa Yehova paguwa lansembe+ la Yehova limene iye anamanga patsogolo pa khonde.+

  • 2 Mbiri 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kuwonjezera pamenepo, Solomo anasankha magulu a ansembe+ kuti azitumikira mogwirizana ndi lamulo la Davide bambo ake. Anasankhanso Alevi kuti azikhala pamalo awo a ntchito nʼkumatamanda+ ndi kutumikira pamaso pa ansembe mogwirizana ndi dongosolo la tsiku ndi tsiku. Komanso anasankha alonda apageti mʼmagulu awo kuti akhale mʼmageti osiyanasiyana+ chifukwa limeneli linali lamulo la Davide munthu wa Mulungu woona.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena