-
Deuteronomo 12:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 “Awa ndi malangizo ndi zigamulo zimene muyenera kutsatira mosamala, masiku onse amene mudzakhale mʼdziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu adzakupatseni kuti likhale lanu.
-
-
Nehemiya 9:34Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
34 Mafumu athu, akalonga athu, ansembe athu ndi makolo athu sanatsatire Chilamulo chanu ndipo sanamvere malamulo anu kapena zikumbutso zanu zowachenjeza.
-