Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aisiraeli onse analembedwa pamndandanda wa mayina wotsatira makolo awo mʼBuku la Mafumu a Isiraeli. Ndipo Ayuda anatengedwa kupita ku ukapolo ku Babulo chifukwa cha kusakhulupirika kwawo.+

  • Ezara 2:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Amene anachokera ku Tele-mela, Tele-harisa, Kerubi, Adoni ndi Imeri, koma sanathe kufotokoza mzere wa makolo awo ndi kumene anachokera komanso kuti anali Aisiraeli kapena ayi, ndi awa:+

  • Ezara 2:62
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Amenewa ndi amene mayina awo anawayangʼana mʼkaundula kuti atsimikizire anthu onse za mzere wawo wobadwira koma sanapezekemo. Choncho anawaletsa kuti asatumikire ngati ansembe.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena