-
Ezara 2:2-35Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Amenewa anabwera pamodzi ndi Zerubabele,+ Yesuwa,*+ Nehemiya, Seraya, Reelaya, Moredikayi, Bilisani, Misipara, Bigivai, Rehumu ndi Bana.
Chiwerengero cha amuna a Isiraeli chinali ichi:+ 3 Ana a Parosi, 2,172. 4 Ana a Sefatiya, 372. 5 Ana a Ara,+ 775. 6 Ana a Pahati-mowabu,+ ochokera mwa ana a Yesuwa ndi Yowabu, 2,812. 7 Ana a Elamu,+ 1,254. 8 Ana a Zatu,+ 945. 9 Ana a Zakai, 760. 10 Ana a Bani, 642. 11 Ana a Bebai, 623. 12 Ana a Azigadi, 1,222. 13 Ana a Adonikamu, 666. 14 Ana a Bigivai, 2,056. 15 Ana a Adini, 454. 16 Ana a Ateri, a mʼbanja la Hezekiya, 98. 17 Ana a Bezai, 323. 18 Ana a Yora, 112. 19 Ana a Hasumu,+ 223. 20 Ana a Gibara, 95. 21 Ana a Betelehemu, 123. 22 Amuna a ku Netofa, 56. 23 Amuna a ku Anatoti,+ 128. 24 Ana a Azimaveti, 42. 25 Ana a Kiriyati-yearimu, Kefira ndi Beeroti, 743. 26 Ana a Rama+ ndi Geba,+ 621. 27 Amuna a ku Mikemasi, 122. 28 Amuna a ku Beteli ndi a ku Ai,+ 223. 29 Ana a Nebo,+ 52. 30 Ana a Magabisi, 156. 31 Ana a Elamu wina, 1,254. 32 Ana a Harimu, 320. 33 Ana a Lodi, Hadidi ndi Ono, 725. 34 Ana a Yeriko, 345. 35 Ana a Senaya, 3,630.
-