Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 6:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mʼmasiku amenewo, anthu olemekezeka+ a mu Yuda ankalemba makalata ambiri opita kwa Tobia ndipo Tobiayo ankawayankha. 18 Anthu ambiri mu Yuda anamulumbirira kuti akhala kumbali yake chifukwa anali mkamwini wa Sekaniya, mwana wa Ara.+ Ndipo Yehohanani mwana wa Tobia anakwatira mwana wamkazi wa Mesulamu,+ mwana wa Berekiya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena