Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno Nehemiya, yemwe pa nthawiyo anali bwanamkubwa,* Ezara+ wansembe ndi wokopera Malemba,* komanso Alevi amene ankapereka malangizo kwa anthu, anauza anthuwo kuti: “Lero ndi tsiku lopatulika kwa Yehova Mulungu wanu.+ Musakhale achisoni ndipo musalire.” Ananena zimenezi chifukwa anthu onse ankalira pamene ankamvetsera mawu a mʼChilamulocho.

  • Nehemiya 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Amene anatsimikizira panganoli ndi chidindo chawo+ anali awa:

      Nehemiya amene anali bwanamkubwa,* mwana wa Hakaliya,

      Zedekiya,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena