Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma iwe Danieli upirire mpaka mapeto ndipo udzapuma. Ndiyeno pamapeto amasikuwo udzauka kuti ulandire gawo lako.”+

  • Yohane 5:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Musadabwe nazo zimenezi, chifukwa nthawi ikubwera imene onse amene ali mʼmanda achikumbutso adzamva mawu ake+ 29 ndipo adzatuluka. Amene ankachita zabwino adzauka kuti alandire moyo ndipo amene ankachita zoipa adzauka kuti aweruzidwe.+

  • Yohane 11:43, 44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Atanena zimenezi, anafuula mokweza mawu kuti: “Lazaro, tuluka!”+ 44 Munthu amene anali wakufa uja anatuluka. Mapazi ndi manja ake anali okulungidwa ndi nsalu zamaliro, nkhope yakenso inali yomanga ndi nsalu. Ndiyeno Yesu anawauza kuti: “Mʼmasuleni kuti athe kuyenda.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena