Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anzake atatu a Yobu anamva za masoka onse amene anamugwera ndipo aliyense wa iwo anabwera kuchokera kwawo. Mayina awo anali Elifazi+ wa ku Temani, Bilidadi+ wa ku Shuwa+ ndi Zofari+ wa ku Naama. Iwo anapangana kuti akumane kuti apite akatonthoze Yobu ndi kumulimbikitsa.

  • Yobu 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Elifazi+ wa ku Temani anayankha kuti:

  • Yobu 22:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Elifazi+ wa ku Temani anayankha kuti:

  • Yobu 42:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova atanena mawu amenewa kwa Yobu, Yehova anauza Elifazi wa ku Temani kuti:

      “Mkwiyo wanga wayakira iweyo ndi anzako awiriwo,+ chifukwa simunanene zoona za ine,+ ngati mmene wachitira mtumiki wanga Yobu.

  • Yobu 42:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho Elifazi wa ku Temani, Bilidadi wa ku Shuwa ndi Zofari wa ku Naama anapita nʼkukachita zimene Yehova anawauza. Ndipo Yehova anamva pemphero la Yobu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena