Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Usamadzione kuti ndiwe wanzeru.+

      Uziopa Yehova ndi kupatuka pa choipa.

  • Mateyu 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pa nthawi imeneyo Yesu ananena kuti: “Ndikukutamandani inu Atate pamaso pa onse, Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi, chifukwa anthu anzeru ndi ozindikira mwawabisira zinthu zimenezi ndipo mwaziulula kwa ana aangʼono.+

  • Aroma 11:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zimenezo nʼzoona. Iwo anadulidwa chifukwa analibe chikhulupiriro,+ koma iweyo udakali wolumikizidwa kumtengowo chifukwa cha chikhulupiriro.+ Chotsa maganizo odzikuzawo, koma khala ndi mantha.

  • Aroma 12:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Muziona ena mmene inuyo mumadzionera. Musamaganize modzikuza, koma khalani ndi mtima wodzichepetsa.+ Musamadzione ngati anzeru.+

  • 1 Akorinto 1:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mukuona mmene anakuitanirani abale, kuti si ambiri amene anthu amawaona kuti ndi anzeru+ omwe anaitanidwa, si ambiri amphamvu amene anaitanidwa, si ambiri a mʼmabanja olemekezeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena