Salimo 49:6, 7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Anthu amene akukhulupirira chuma chawo,+Amene amadzitamandira chifukwa cha kuchuluka kwa chuma chawo,+ 7 Palibe ngakhale mmodzi wa iwo amene angathe kuwombola mʼbale wake,Kapena kumuperekera dipo kwa Mulungu,+ Miyambo 11:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Munthu amene amadalira chuma chake adzakumana ndi mavuto,+Koma anthu olungama adzasangalala ngati mtengo wa masamba obiriwira.+
6 Anthu amene akukhulupirira chuma chawo,+Amene amadzitamandira chifukwa cha kuchuluka kwa chuma chawo,+ 7 Palibe ngakhale mmodzi wa iwo amene angathe kuwombola mʼbale wake,Kapena kumuperekera dipo kwa Mulungu,+ Miyambo 11:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Munthu amene amadalira chuma chake adzakumana ndi mavuto,+Koma anthu olungama adzasangalala ngati mtengo wa masamba obiriwira.+
28 Munthu amene amadalira chuma chake adzakumana ndi mavuto,+Koma anthu olungama adzasangalala ngati mtengo wa masamba obiriwira.+