Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 49:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anthu amene akukhulupirira chuma chawo,+

      Amene amadzitamandira chifukwa cha kuchuluka kwa chuma chawo,+

       7 Palibe ngakhale mmodzi wa iwo amene angathe kuwombola mʼbale wake,

      Kapena kumuperekera dipo kwa Mulungu,+

  • Miyambo 11:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Munthu amene amadalira chuma chake adzakumana ndi mavuto,+

      Koma anthu olungama adzasangalala ngati mtengo wa masamba obiriwira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena