Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndimadalira Mulungu, ndimamutamanda chifukwa cha mawu ake.

      Ine ndimadalira Mulungu, sindikuopa.

      Kodi munthu wamba angandichite chiyani?+

  • Yesaya 51:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndimvereni, inu anthu amene mumadziwa chilungamo,

      Inu anthu amene chilamulo changa chili* mumtima mwanu.+

      Musachite mantha ndi mawu otonza amene anthu akunena

      Ndipo musaope chifukwa cha mawu awo onyoza.

  • Yesaya 51:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Ineyo ndi amene ndikukutonthoza.+

      Ndiye nʼchifukwa chiyani ukuopa munthu woti adzafa+

      Ndiponso mwana wa munthu amene adzanyale ngati udzu wobiriwira?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena