Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 108:2-5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Dzuka, iwe choimbira cha zingwe, ndi iwenso zeze.+

      Ine ndidzadzuka mʼbandakucha.

       3 Ndidzakutamandani pakati pa mitundu ya anthu, inu Yehova.

      Ndidzaimba nyimbo zokutamandani pakati pa mitundu ya anthu.

       4 Chifukwa chikondi chanu chokhulupirika nʼchachikulu moti chafika kumwamba,+

      Ndipo kukhulupirika kwanu kwafika kuthambo.

       5 Inu Mulungu, kwezekani kupitirira kumwamba.

      Ulemerero wanu ukhale padziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena