Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kenako Sauli anauza mwana wake Yonatani komanso atumiki ake onse kuti akufuna kupha Davide.+

  • Salimo 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Amadikirira anthu pamalo amene iye amabisala ngati mkango umene uli pamalo ake amene umabisala.*+

      Amadikirira kuti agwire munthu wovutika.

      Amagwira munthu wovutikayo pomukulunga ndi ukonde wake.+

  • Salimo 71:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Adani anga amandinenera zoipa,

      Ndipo anthu amene akufuna kuchotsa moyo wanga, amandikonzera chiwembu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena