Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova anawonjezera kuti: “Ndaona mmene anthu anga amene ali ku Iguputo akuvutikira, ndipo ndamva kulira kwawo chifukwa cha amene akuwagwiritsa ntchito mwankhanza. Ndikudziwa bwino ululu umene akumva.+

  • Salimo 72:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Adzamvera chisoni munthu wonyozeka ndi wosauka,

      Ndipo adzapulumutsa miyoyo ya anthu osauka.

      14 Adzawapulumutsa* kuti asaponderezedwe komanso kuchitiridwa zachiwawa,

      Ndipo adzaona kuti magazi awo ndi amtengo wapatali.

  • Luka 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiye kodi Mulungu sadzaonetsetsa kuti chilungamo chachitika kwa osankhidwa ake, amene amafuulira kwa iye masana ndi usiku,+ pamene akuwalezera mtima?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena