Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 3:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Onyamula Likasawo atangofika pamtsinje wa Yorodano, nʼkuponda madzi a mʼmphepete mwake (mtsinje wa Yorodano unkasefukira+ nyengo yonse yokolola), 16 madzi ochokera kumtunda anaima ngati khoma. Ndipo anakhala ngati damu lomwe linasefukira mpaka kukafika kutali kwambiri. Izi zinachitikira ku Adamu, mzinda woyandikana ndi mzinda wa Zeretani. Koma madzi akumunsi omwe ankapita kunyanja ya Araba, yomwe ndi Nyanja Yamchere,* anaphwa. Choncho, madzi a mtsinjewo anagawikana, ndipo anthuwo anawolokera kutsidya lina, pafupi ndi Yeriko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena