Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 27:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kodi munthu woipa* akawonongedwa amakhala ndi chiyembekezo chilichonse,+

      Mulungu akachotsa moyo wake?

       9 Kodi Mulungu adzamva kulira kwake

      Mavuto akadzamugwera?+

  • Miyambo 15:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Yehova ali kutali ndi anthu oipa,

      Koma amamva pemphero la anthu olungama.+

  • Miyambo 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Munthu amene amakana kumvera chilamulo,

      Ngakhale pemphero lake limakhala lonyansa.+

  • Yesaya 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo mukatambasula manja anu,

      Ndimakubisirani maso anga.+

      Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+

      Ine sindimvetsera.+

      Manja anu adzaza magazi.+

  • Yohane 9:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Tikudziwa kuti Mulungu samvetsera ochimwa,+ koma ngati munthu amaopa Mulungu ndipo amachita chifuniro chake, munthu ameneyo amamumvetsera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena