-
1 Mafumu 4:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Ayuda ndi Aisiraeli ankakhala mwamtendere. Aliyense ankakhala pansi pa mtengo wake wa mpesa ndi mtengo wake wa mkuyu, kuchokera ku Dani mpaka ku Beere-seba, masiku onse a Solomo.
-
-
Yesaya 2:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Mulungu adzaweruza anthu a mitundu yosiyanasiyana
Ndipo adzakonza zinthu zimene ndi zolakwika pakati pawo.
Iwo adzasula malupanga awo kuti akhale makasu a pulawo,
Ndipo mikondo yawo adzaisula kuti ikhale zida zosadzira mitengo.+
Mtundu wa anthu sudzanyamula lupanga kuti umenyane ndi mtundu unzake,
Ndipo anthuwo sadzaphunziranso nkhondo.+
-