Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 106:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pa nthawiyo iwo ananyoza dziko losiririka,+

      Ndipo analibe chikhulupiriro pa zimene anawalonjeza.+

  • Aheberi 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nʼchifukwa chake ndinanyansidwa ndi mʼbadwo umenewo, ndipo ndinati, ‘Mitima yawo imasochera nthawi zonse ndipo njira zanga sakuzidziwa.’

  • Yuda 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ngakhale kuti mukudziwa kale zonsezi, ndikufuna kukukumbutsani kuti Yehova* atapulumutsa anthu ake powatulutsa mʼdziko la Iguputo,+ pambuyo pake anawononga amene analibe chikhulupiriro.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena