Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Komabe anthu onse amene aona ulemerero wanga ndi zizindikiro zanga+ zimene ndinachita ku Iguputo, komanso zimene ndachita mʼchipululu, koma apitiriza kundiyesa+ maulendo 10 onsewa, ndipo sanamvere mawu anga,+

  • Deuteronomo 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova Mulungu wanu musamamuyese+ ngati mmene munamuyesera ku Masa.+

  • Salimo 95:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Musaumitse mitima yanu ngati mmene makolo anu anachitira ku Meriba,*+

      Ngati mmene anachitira ku Masa* mʼchipululu,+

       9 Pamene makolo anu anandiyesa.+

      Iwo anatsutsana ndi ine ngakhale kuti anaona ntchito zanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena