Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo anasiya Yehova, Mulungu wa makolo awo amene anawatulutsa mʼdziko la Iguputo+ nʼkuyamba kutsatira milungu ya anthu owazungulira.+ Anayamba kugwadira milunguyo ndipo anakhumudwitsa Yehova.+

  • 1 Samueli 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako Samueli anauza Aisiraeli onse kuti: “Ngati mukubwereradi kwa Yehova ndi mtima wanu wonse,+ chotsani milungu yachilendo+ komanso zifaniziro za Asitoreti,+ ndipo muzitumikira Yehova yekha ndi mtima wanu wonse.+ Mukatero, adzakupulumutsani mʼmanja mwa Afilisiti.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena