Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ukauze Farao kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Isiraeli ndi mwana wanga wamwamuna, mwana wanga woyamba kubadwa.+

  • Yesaya 49:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndiyeno Yehova amene anandipanga ndili mʼmimba kuti ndikhale mtumiki wake,

      Wandiuza kuti nditenge Yakobo nʼkumubwezera kwa iye,

      Nʼcholinga choti Isiraeli asonkhanitsidwe kwa iye.+

      Ine ndidzalemekezedwa pamaso pa Yehova

      Ndipo Mulungu wanga adzakhala mphamvu yanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena