Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 1:8-10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Patapita nthawi, mfumu ina yomwe sinkamudziwa Yosefe inayamba kulamulira ku Iguputo. 9 Mfumuyo inauza anthu ake kuti: “Taonani! Aisiraeli achuluka kwambiri ndipo ndi amphamvu kuposa ife.+ 10 Tiyeni tiwachenjerere anthu amenewa kuti asapitirize kuchulukana, kuopera kuti pa nthawi ya nkhondo angadzagwirizane ndi adani athu nʼkumenyana nafe kenako nʼkuchoka mʼdziko muno.”

  • 2 Mbiri 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Amowabu,+ Aamoni+ ndi Aamonimu* ena anabwera kudzamenyana ndi Yehosafati.

  • Esitere 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma Hamani anaona kuti nʼzosakwanira kupha Moredikayi yekha chifukwa anthu anali atamuuza za anthu a mtundu wa Moredikayi. Choncho Hamani anaganiza zoti aphe Ayuda onse, anthu a mtundu wa Moredikayi mʼmadera onse amene Ahasiwero ankalamulira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena