Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye adzawauza kuti: “Inetu ndasankha mfumu yanga+

      Ndipo ikulamulira ku Ziyoni,+ phiri langa lopatulika.”

  • Salimo 24:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndi ndani angakwere kuphiri la Yehova,+

      Ndipo ndi ndani angaime mʼmalo ake opatulika?

       4 Aliyense amene ndi wosalakwa komanso wopanda chinyengo mumtima mwake,+

      Amene sanalumbire mwachinyengo potchula moyo Wanga,*

      Kapena kulumbira pofuna kupusitsa anthu ena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena