Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nahumu 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova ndi Mulungu amene amafuna kuti anthu azidzipereka kwa iye yekha+ ndipo amabwezera adani ake.

      Yehova amabwezera adani ake ndipo ndi wokonzeka kusonyeza mkwiyo wake.+

      Yehova amabwezera adani ake,

      Ndipo adani ake amawasungira mkwiyo.

  • Nahumu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye atapsa mtima, ndani angaime pamaso pake?+

      Iye atakwiya, ndani angalimbe mtima kuima pamaso pake?+

      Mkwiyo wake adzaukhuthula ngati moto,

      Ndipo miyala idzaphwanyidwa chifukwa cha iye.

  • Malaki 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Taonani! Tsiku loyaka ngati ngʼanjo likubwera,+ ndipo anthu onse odzikuza ndi onse ochita zoipa adzakhala ngati mapesi. Pa tsikulo iwo adzawonongedwa moti sipadzatsala mizu kapena nthambi zawo,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena