Salimo 12:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Yehova wanena kuti: “Chifukwa chakuti ovutika akuponderezedwaChifukwa cha kuusa moyo kwa anthu osauka,+Ndidzanyamuka nʼkuchitapo kanthu, Ndidzawapulumutsa kwa anthu amene akuwanyoza.”* Miyambo 22:22, 23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Usabere munthu wosauka chifukwa choti ndi wosauka,+Ndipo usapondereze munthu wonyozeka pageti la mzinda,+23 Chifukwa Yehova adzawateteza pa mlandu wawo,+Ndipo adzachotsa moyo wa anthu amene akuwabera mwachinyengo. Yakobo 5:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Tamverani! Malipiro amene simunapereke kwa anthu amene anagwira ntchito yokolola mʼminda yanu akufuula ndipo Yehova* wa magulu ankhondo akumwamba wamva kufuula kopempha thandizo kwa anthu okololawo.+
5 Yehova wanena kuti: “Chifukwa chakuti ovutika akuponderezedwaChifukwa cha kuusa moyo kwa anthu osauka,+Ndidzanyamuka nʼkuchitapo kanthu, Ndidzawapulumutsa kwa anthu amene akuwanyoza.”*
22 Usabere munthu wosauka chifukwa choti ndi wosauka,+Ndipo usapondereze munthu wonyozeka pageti la mzinda,+23 Chifukwa Yehova adzawateteza pa mlandu wawo,+Ndipo adzachotsa moyo wa anthu amene akuwabera mwachinyengo.
4 Tamverani! Malipiro amene simunapereke kwa anthu amene anagwira ntchito yokolola mʼminda yanu akufuula ndipo Yehova* wa magulu ankhondo akumwamba wamva kufuula kopempha thandizo kwa anthu okololawo.+