Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Mumakulitsa njira kuti mapazi anga azidutsamo,

      Ndipo mapazi anga sadzaterereka.+

  • Salimo 94:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene ndinanena kuti: “Phazi langa likuterereka,”

      Chikondi chanu chokhulupirika, inu Yehova, chinapitiriza kundithandiza.+

  • Salimo 119:133
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 133 Nditsogolereni ndi mawu anu kuti ndiyende mʼnjira yotetezeka.

      Musalole kuti choipa chilichonse chindilamulire.+

  • Salimo 121:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye sadzalola kuti phazi lako literereke.*+

      Amene akukuyangʼanira sadzawodzera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena