Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iwo anachitadi zomwezo. Aroni anatambasula dzanja lake nʼkumenya fumbi lapansi ndi ndodo yake, ndipo tizilomboto tinayamba kusowetsa mtendere anthu ndi nyama zomwe. Fumbi lonse lamʼdziko la Iguputo linasanduka tizilombo toyamwa magazi.+

  • Ekisodo 8:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Yehova anachitadi zimenezi, moti ntchentche zoluma zinali paliponse mʼnyumba ya Farao, mʼnyumba za atumiki ake ndi mʼdziko lonse la Iguputo.+ Ntchentchezo+ zinabweretsa mavuto aakulu kwa anthu a ku Iguputo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena