Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:31-33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 ‘Phokoso lidzamveka kumalekezero a dziko lapansi,

      Chifukwa Yehova akufuna kuimba mlandu mitundu ya anthu.

      Iye adzapereka yekha chiweruzo kwa anthu onse.+

      Ndipo anthu oipa adzawapha ndi lupanga,’ akutero Yehova.

      32 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti:

      ‘Taonani! Tsoka likufalikira kuchokera ku mtundu wina kupita ku mtundu wina,+

      Ndipo mkuntho wamphamvu udzafika kuchokera kumadera akutali kwambiri a dziko lapansi.+

      33 Pa tsiku limenelo anthu amene adzaphedwe ndi Yehova adzachokera kumalekezero a dziko lapansi kukafika kumalekezero ena a dziko lapansi. Maliro awo sadzaliridwa, sadzawasonkhanitsa pamodzi kapena kuwaika mʼmanda. Iwo adzakhala ngati manyowa panthaka.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena