Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 11:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Komabe tikaweruzidwa, ndiye kuti Yehova* watiphunzitsa+ kuti tisalandire chilango limodzi ndi dziko.+

  • Aheberi 12:9-11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Bambo athu otibereka ankatilanga ndipo tinkawalemekeza. Ndiye kuli bwanji Atate wa moyo wathu wauzimu? Kodi sitiyenera kuwagonjera koposa pamenepo kuti tikhale ndi moyo?+ 10 Chifukwa bambo athu otiberekawo, anatilanga kwa nthawi yochepa mogwirizana ndi zimene ankaziona kuti nʼzoyenera, koma Mulungu amatilanga kuti zinthu zitiyendere bwino ndiponso kuti tikhale oyera ngati iyeyo.+ 11 Nʼzoona kuti palibe chilango chimene chimakhala chosangalatsa pa nthawi yomwe ukuchilandira, koma chimakhala chowawa. Komabe pambuyo pake, kwa anthu amene aphunzirapo kanthu pa chilangocho, chimabala chipatso chamtendere, chomwe ndi chilungamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena