Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 86:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Tetezani moyo wanga chifukwa ndine wokhulupirika.+

      Pulumutsani mtumiki wanu amene amakukhulupirirani,

      Chifukwa ndinu Mulungu wanga.+

  • Yesaya 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Usachite mantha, chifukwa ndili ndi iwe.+

      Usade nkhawa chifukwa ine ndine Mulungu wako.+

      Ndikulimbitsa, ndithu ndikuthandiza,+

      Ndikugwira mwamphamvu ndi dzanja langa lamanja lachilungamo.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena