Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 139:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mumandiona* ndikamayenda komanso ndikagona.

      Mumadziwa chilichonse chimene ndikuchita.+

  • Miyambo 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa maso a Yehova amaona chilichonse chimene munthu akuchita,

      Ndipo iye amafufuza njira zake zonse.+

  • Miyambo 15:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngati Yehova amaona bwinobwino amene ali mʼManda* ndiponso malo achiwonongeko,*+

      Ndiye kuli bwanji zimene zili mʼmitima ya anthu?+

  • Aheberi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Palibe cholengedwa chimene Mulungu sangathe kuchiona.+ Chifukwa kwa iye zinthu zonse zili poonekera ndipo amatha kuziona bwinobwino moti ifeyo tidzayankha kwa Mulunguyo pa zochita zathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena