-
2 Samueli 22:26-31Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Munthu wokhulupirika, mumamuchitira mokhulupirika.+
Munthu wamphamvu komanso wosalakwa, mumamuchitira mwachilungamo.+
27 Munthu woyera, mumamusonyeza kuti ndinu woyera,+
Koma munthu wamaganizo opotoka mumamusonyeza kuti ndinu wochenjera.+
30 Ndi thandizo lanu ndingalimbane ndi gulu la achifwamba;
Ndi mphamvu za Mulungu ndingakwere khoma.+
Iye ndi chishango kwa onse othawira kwa iye.+
-