Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 30:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa pa munthu,+

      Koma munthu amene wasangalala naye* amamukomera mtima kwa moyo wake wonse.+

      Munthu akhoza kulira usiku, koma mʼmawa amafuula mosangalala.+

  • Yesaya 61:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Mzimu wa Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, uli pa ine,+

      Chifukwa Yehova anandidzoza kuti ndilengeze uthenga wabwino kwa anthu ofatsa.+

      Anandituma kuti ndikamange mabala a anthu osweka mtima,

      Kuti ndilengeze za ufulu kwa anthu amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina,

      Komanso kuti maso a akaidi adzatsegulidwa.+

       2 Wandituma kuti ndilengeze za chaka cha Yehova chokomera anthu mtima,*

      Ndi za tsiku lobwezera la Mulungu wathu,+

      Komanso kuti nditonthoze anthu onse amene akulira,+

       3 Kuti ndisamalire anthu onse amene akulirira Ziyoni,

      Kuti ndiwapatse nsalu yovala kumutu mʼmalo mwa phulusa,

      Kuti ndiwapatse mafuta kuti azisangalala mʼmalo molira,

      Kuti ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda mʼmalo mokhala otaya mtima.

      Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ikuluikulu ya chilungamo,

      Yodzalidwa ndi Yehova kuti iyeyo alemekezedwe.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena