Yobu 26:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Manda* ali maliseche pamaso pa Mulungu,+Ndipo malo achiwonongeko* amakhala osavundikira. Miyambo 15:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ngati Yehova amaona bwinobwino amene ali mʼManda* ndiponso malo achiwonongeko,*+ Ndiye kuli bwanji zimene zili mʼmitima ya anthu?+
11 Ngati Yehova amaona bwinobwino amene ali mʼManda* ndiponso malo achiwonongeko,*+ Ndiye kuli bwanji zimene zili mʼmitima ya anthu?+