Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Usadzudzule wonyoza chifukwa angadane nawe.+

      Dzudzula munthu wanzeru ndipo adzakukonda.+

  • Miyambo 19:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Menya munthu wonyoza+ kuti wosadziwa zinthu achenjere,+

      Ndipo dzudzula munthu womvetsa zinthu kuti awonjezere zimene akudziwa.+

  • Miyambo 25:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Munthu wanzeru akamadzudzula munthu wa khutu lomvetsera+

      Amakhala ngati ndolo yagolide ndiponso ngati chokongoletsera chagolide woyenga bwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena